LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb20 September tsa. 2
  • Usatsatile Khamu la Anthu

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Usatsatile Khamu la Anthu
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
  • Nkhani Zofanana
  • Khamu Lalikulu Losaŵelengeka Likudalitsidwa na Yehova
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
  • Muzikhala Okonzeka Kukhululukila Ena
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
  • “Taonani! “Khamu Lalikulu la Anthu”
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2019
  • Mmene Mungasankhile Zosangulutsa Zabwino
    “Khalanibe m’Cikondi ca Mulungu”
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
mwb20 September tsa. 2
Amuna ndi akazi atamba nyuzi pa foni na pa TV ikulu ku malo kuli anthu ambili.

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | EKSODO 23-24

Usatsatile Khamu la Anthu

23:1-3

Yehova anacenjeza mboni na oweluza kuti pa milandu asamasonkhezeledwe na khamu la anthu kuti apeleke umboni wabodza kapena kuweluza mopanda cilungamo. Mfundo imeneyi ya kusatsatila khamu la anthu igwilanso nchito m’mbali zina za umoyo wathu. Nthawi zonse dzikoli limalimbikitsa Akhristu kuti aziganiza na kucita zinthu m’njila imene anthu osalemekeza Yehova amacitila.—Aroma 12:2.

N’cifukwa ciani si canzelu kutsatila khamu la anthu pamene

  • tamvela nkhani zopanda umboni kapena mijedo?

  • tisankha zovala, makonzedwe a tsitsi, komanso zosangalatsa?

  • tiganizila na kucita zinthu ndi anthu osiyana nawo mtundu, cikhalidwe, kapena zacuma?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani