LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb19 December tsa. 6
  • “Taonani! Zinthu Zonse Zimene Ndikupanga N’zatsopano”

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • “Taonani! Zinthu Zonse Zimene Ndikupanga N’zatsopano”
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
  • Nkhani Zofanana
  • Kumwamba Kwatsopano ndi Dziko Lapansi Latsopano Zidzabweletsa Cisangalalo Cacikulu
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
  • Mavuto Adzatha Posacedwapa!
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2013
  • Zamkatimu
    Galamuka!—2022
  • Yehova Analenga Zamoyo pa Dziko Lapansi
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
mwb19 December tsa. 6
Zipupa za Yerusalemu Watsopano n’zomangidwa na miyala ya yasipi, ndipo mzindawo ni wa golide woyengedwa bwino monga gilasi

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | CHIVUMBULUTSO 20-22

“Taonani! Zinthu Zonse Zimene Ndikupanga N’zatsopano”

21:1-5

Yehova walonjeza kuti adzapanga zinthu zonse kukhala zatsopano.

  • “Kumwamba kwatsopano”: Boma latsopano limene lidzabweletsa cilungamo na kukonza zinthu zonse pa padziko lapansi

  • “Dziko lapansi latsopano”: Anthu amene amagonjela ulamulilo wa Mulungu na kutsatila miyezo yake yolungama

  • “Zinthu zonse . . . n’zatsopano”: Mavuto onse na nkhaŵa zidzalowedwa m’malo na maganizo osangalatsa tsiku lilonse

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani