LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb20 February tsa. 4
  • Yehova Anasintha Dzina la Abulamu na Sarai—Cifukwa?

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Yehova Anasintha Dzina la Abulamu na Sarai—Cifukwa?
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
  • Nkhani Zofanana
  • Mulungu Anamucha Mfumukazi
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawila)—2017
  • “Ndiwe Mkazi Wokongola m’Maonekedwe Ako”
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawila)—2017
  • Mpaka Anakhala na Mwana Wake!
    Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
mwb20 February tsa. 4

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | GENESIS 15-17

“Yehova Anasintha Dzina la Abulamu na Sarai—Cifukwa?”

17:1, 3-5, 15, 16

Yehova anaona Abulamu kukhala wopanda colakwa pamaso pake. Atafotokoza zowonjezeleka zokhudza lonjezo lake kwa Abulamu, Mulungu anapatsa Abulamu na Sarai maina okhala na matanthauzo a ulosi.

Mogwilizana na maina awo, Abulahamu anakhala Tate wa mitundu yambili, ndipo Sara anakhala kholo la mafumu.

  • Abulahamu.

    Abulahamu

    Tate wa Khamu

  • Sara.

    Sara

    Mfumukazi

Zithunzi: Mlongo wacicepele akupita patsogolo mwauzimu. 1. Akubatizika. 2. Akukamba nkhani pa msonkhano wa mkati mwa wiki. 3. Ali mu ulaliki, ndipo akutambitsa mayi wina vidiyo.

Pobadwa, sitidzisankhila tekha dzina limene tidzapatsidwa. Koma mofanana na Abulahamu na Sara, tingadzipangile tekha dzina labwino. Dzifunseni kuti:

  • ‘Kodi ningacite ciani kuti Yehova aziniona kukhala wopanda colakwa?’

  • Kodi nikupanga dzina lotani kwa Yehova?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani