LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb20 March tsa. 3
  • Mkazi wa Isaki

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Mkazi wa Isaki
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
  • Nkhani Zofanana
  • Cikhulupililo Ciyesedwa
    Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
  • Mulungu Ayesa Cikhulupililo Ca Abulahamu
    Buku Langa La Nkhani Za M’baibo
  • Isaki Apeza Mkazi Wabwino
    Buku Langa La Nkhani Za M’baibo
  • “Mulungu . . . Anamuyesa Abulahamu”
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
mwb20 March tsa. 3
Rabeka akuthila madzi m’comwelamo ziŵeto kuti ngamila zimwe. Mtumiki wa Abulahamu akumuyang’ana capatali.

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | GENESIS 24

Mkazi wa Isaki

24:2-4, 11-15, 58, 67

Mtumiki wa Abulahamu anapempha Yehova kuti amuthandize kusankha mkazi wa Isaki. (Gen. 24:42-44) Na ife tifunika kupempha citsogozo ca Yehova tisanapange zosankha zikulu-zikulu. Motani?

  • Pemphelani

  • Fufuzani m’Mawu a Mulungu na m’zofalitsa zathu

  • Pemphani thandizo kwa Akhristu ofikapo kuuzimu

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani