LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb20 June tsa. 2
  • Yosefe Anakhululukila Abale Ake

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Yosefe Anakhululukila Abale Ake
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
  • Nkhani Zofanana
  • Muzikhala Okonzeka Kukhululukila Ena
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
  • Yehova Sanamuiŵale Yosefe
    Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
  • Yehova Ni Wokonzeka Kukhululuka
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2022
  • Abale Ake Amuzonda Yosefe
    Buku Langa La Nkhani Za M’baibo
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
mwb20 June tsa. 2
Yosefe akudziulula kwa abale ake ndipo iwo akumuyang’ana mwacidwi.

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | GENESIS 44-45

Yosefe Anakhululukila Abale Ake

44:1, 2, 33, 34; 45:4, 5

Zingakhale zovuta kukhululuka, maka-maka ngati wina anaticitila zinthu zoipa mwadala. Kodi n’ciani cinathandiza Yosefe kukhululukila abale ake pamene anamucitila zinthu zoipa?

  • Yosefe sanafune kuwabwezela, m’malomwake anayetsetsa kuona ngati iwo anasintha popeza anali kufuna kuwakhululukila.—Sal. 86:5; Luka 17:3, 4

  • Yosefe sanapitilize kusunga cakukhosi, m’malomwake anatengela citsanzo ca Yehova amene amakhululukila na mtima wonse. —Mika 7:18, 19

Kodi ningatengele bwanji citsanzo ca Yehova pankhani yokhululukila ena?

Zithunzi: 1. Alongo aŵili akambilana pa Nyumba ya Ufumu. 2. Abale aŵili apatsana moni.
    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani