LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb20 June tsa. 3
  • Thandizo la Cakudya pa Nthawi ya Njala

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Thandizo la Cakudya pa Nthawi ya Njala
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
  • Nkhani Zofanana
  • Mmene Tingagwilitsile Nchito Zinthu Zongomvetsela za pa jw.org
    Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Mafunso Ocokela Kwa Oŵelenga
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2018
  • Gwilitsilani Nchito Webusaiti ya jw.org mu Ulaliki—“Khala Bwenzi la Yehova”
    Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Kabokosi Kakang’ono Kopelekela Cakudya Cauzimu
    Mmene Zopeleka Zanu Zimagwilila Nchito
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
mwb20 June tsa. 3

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | GENESIS 46-47

Thandizo la Cakudya pa Nthawi ya Njala

47:13, 16, 19, 20, 23-25

Yosefe akugwila nchito yoyang’anila cakudya m’dziko la Iguputo. Anthu akubweletsa mathumba a tiligu.

Masiku ano, anthu m’dzikoli ali na njala yauzimu. (Amosi 8:11) Kupitila mwa Khristu Yesu, Yehova amapeleka cakudya cauzimu ca mwana alilenji.

  • Mabuku ophunzilila Baibo

  • Misonkhano ya mpingo

  • Misonkhano yadela komanso yacigawo

  • Zomvetsela

  • Mavidiyo

  • JW.ORG

  • JW Broadcasting

Kodi nimadzimana zinthu ziti kuti nizidya cakudya cauzimu pa tebulo la Yehova nthawi zonse?

M’bale akucititsa Phunzilo la ‘Nsanja ya Mlonda’. Abale na alongo m’gulu akuimika manja kuti apeleke ndemanga.
    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani