LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb20 June tsa. 7
  • “Ine Ndidzakhala Nawe Polankhula”

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • “Ine Ndidzakhala Nawe Polankhula”
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
  • Nkhani Zofanana
  • “Musamade Nkhawa ndi Kanthu Kalikonse”
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
  • Tsanzilani Cikhulupililo ca Mose
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2014
  • Kodi Mumaona “Wosaonekayo”?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2014
  • Citsamba Coyaka Moto
    Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
mwb20 June tsa. 7
Mose na Aroni aonekela pamaso pa Farao na anthu ogwila nchito m’nyumba ya mfumu ya Aiguputo.

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | EKSODO 4-5

“Ine Ndidzakhala Nawe Polankhula”

4:10-15

Ndi thandizo la Yehova, Mose anagonjetsa mantha ake. Kodi tingaphunzilepo ciani pa zimene Yehova anauza Mose?

  • Tizipewa kusumika maganizo athu pa zinthu zimene timalephela kucita

  • Tiyenela kukhala na cidalilo cakuti Yehova adzatipatsa zonse zofunikila kuti tikwanilitse nchito imene tapatsidwa

  • Cikhulupililo cathu mwa Mulungu cidzatithandiza kuti tisamaope anthu

M’bale ateteza cikhulupililo cake pamaso pa khoti.

Kodi Yehova wanithandiza bwanji kupitiliza kulalikila ngakhale panthawi zovuta?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani