LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb20 September tsa. 4
  • Cimene Cinali Cofunika Kwambili m’Cihema

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Cimene Cinali Cofunika Kwambili m’Cihema
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
  • Nkhani Zofanana
  • “Mthunzi wa Zinthu Zabwino Zimene Zikubwela”
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
  • Cihema Colambililako
    Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
  • Yamikilani Mwayi Wanu Wolambila Yehova M’kacisi Wake Wauzimu
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2023
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
mwb20 September tsa. 4
Likasa la cipangano.

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU | EKSODO 25-26

Cimene Cinali Cofunika Kwambili m’Cihema

25:9, 21, 22

Likasa linali cinthu cofunika kwambili m’cihema komanso mu msasa wa Aisiraeli. Kukhalapo kwa Mulungu kunali kuimilidwa na mtambo umene unali pakati pa akelubi, amene anali pa civundikilo ca likasa. Caka ciliconse, pa tsiku la Mwambo Wophimba Macimo, mkulu wa ansembe anali kuloŵa m’malo Oyela Koposa ndipo anali kudontheza magazi a ng’ombe yamphongo na mbuzi patsogolo pa civundikilo kuti aphimbe macimo ya Aisiraeli. (Lev. 16:14, 15) Izi zinali kuimila nthawi pamene Mkulu wa Ansembe Yesu, analowa kumwamba kukapeleka mtengo wake wa dipo pamaso pa Yehova.—Aheb. 9:24-26.

Gwilizanitsani malemba otsatilawa na mapindu amene tili nawo cifukwa ca nsembe:

MALEMBA

  • 1 Yoh. 1:8, 9

  • Aheb. 9:13, 14

  • Aroma 6:23

MAPINDU

  • ciyembekezo ca moyo wosatha

  • kukhululukidwa macimo

  • cikumbumtima coyela

Kodi tifunika kucita ciani kuti tipeze mapindu amenewa?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani