LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb22 May tsa. 5
  • “Cikondi . . . Sicikondwela ndi Zosalungama”

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • “Cikondi . . . Sicikondwela ndi Zosalungama”
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
  • Nkhani Zofanana
  • Akhristu Oona Amadziŵika na Cikondi—Kondwelani na Coonadi
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
  • Yonatani, Munthu Wolimba Mtima Komanso Wokhulupilika
    Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
  • Cifukwa Cake Davide Afunikila Kuthaŵa
    Buku Langa La Nkhani Za M’baibo
  • Davide na Sauli
    Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
mwb22 May tsa. 5

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

“Cikondi . . . Sicikondwela ndi Zosalungama”

Akhristu oona amalola cikondi kuwatsogolela pa zocita zawo zonse. Cikondi “sicikondwela ndi zosalungama.” (1 Akor. 13:4, 6) Conco, timapewa zosangalatsa zimene zimaonetsa kuti zinthu monga zaciwelewele komanso zaciwawa n’zabwino. Komanso, sitikondwela ena akakumana na mavuto, ngakhale anthu amene anatilakwila. —Miy. 17:5.

ONELELANI VIDIYO YAKUTI KUMBUKILANI MMENE CIKONDI CILILI—SICIKONDWELA NDI ZOSALUNGAMA, NDIYENO YANKHANI MAFUNSO OTSATILAWA:

  • Kodi Davide anamvela bwanji atadziŵa kuti Sauli na Yonatani afa?

  • Kodi Davide anaimba nyimbo yotani polila Sauli na Yonatani?

  • N’cifukwa ciyani Davide sanakondwele na imfa ya Sauli?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani