LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb22 November tsa. 8
  • Kucita Zinthu na Mtima Wonse Kumabweletsa Madalitso Oculuka

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Kucita Zinthu na Mtima Wonse Kumabweletsa Madalitso Oculuka
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
  • Nkhani Zofanana
  • Zimene Adani Athu Amacita Poyesa Kutifooketsa
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
  • Ife Tili ndi Ambili Kuposa Amene Ali ndi Iwo
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
  • Mayi Woipa Komanso Wofunitsitsa Ulamulilo Analangidwa
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
  • Yehova Amatidalitsa Ngati Ticita Zinthu Zoonetsa Cikhulupililo
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2021
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
mwb22 November tsa. 8
Elisa ni wodwala ndipo ali pabedi. Iye akupeleka malangizo kwa Mfumu Yehoasi. Yehoasi wagwila mivi inayi m’manja mwake.

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Kucita Zinthu na Mtima Wonse Kumabweletsa Madalitso Oculuka

Elisa anauza Mfumu Yehoasi kuti acite cina cake coonetsa mmene Aisiraeli adzagonjetsela Asiriya (2 Maf. 13:15-18)

Yehoasi sanacite zinthu na mtima wonse. Ndiye cifukwa cake sanapambane kwenikweni polimbana na adani ake (2 Maf. 13:19; w10 4/15 26 ¶11)

Yehova amawadalitsa kwambili atumiki ake amene amam’funafuna na mtima wonse (Aheb. 11:6; w13 11/1 11 ¶5-6)

DZIFUNSENI KUTI, ‘Kodi nimaonetsa bwanji kuti nimacita zonse zimene ningathe pa zinthu zokhudza kulambila monga kuŵelenga Baibo, kupezeka ku misonkhano, na kulalikila?’

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani