LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb22 November tsa. 10
  • Kuleza Mtima kwa Yehova Kuli na Malile

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Kuleza Mtima kwa Yehova Kuli na Malile
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
  • Nkhani Zofanana
  • Yehova Anapangitsa Zinthu Zosayembekezeleka Kucitika
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
  • Mayi Woipa Komanso Wofunitsitsa Ulamulilo Analangidwa
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
  • Khalanibe Maso
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2023
  • Ife Tili ndi Ambili Kuposa Amene Ali ndi Iwo
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
mwb22 November tsa. 10
Yesu na gulu lake lankhondo lakumwamba akwela mahachi oyela, ndipo akubwela kudzawononga adani a Mulungu padziko lapansi.

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Kuleza Mtima kwa Yehova Kuli na Malile

Yehova analola Asuri kugonjetsa Aisiraeli (2 Maf. 17:5, 6; it-2 908 ¶5)

Yehova anawalanga anthu ake cifukwa anapitiliza kucita zinthu zoipa zomukwiyitsa (2 Maf. 17:9-12; it-1 414-415)

Yehova anawalezela mtima Aisiraeli, ndipo anawacenjeza mobweleza-bweleza (2 Maf. 17:13, 14)

Atate wathu wacikondi wakumwamba ni woleza mtima kwambili na anthu opanda ungwilo. (2 Pet. 3:9) Ngakhale n’conco, kuti akwanilitse colinga cake, posacedwapa adzawononga anthu oipa. N’cifukwa ciyani zimenezi ziyenela kutilimbikitsa kumvela uphungu na kulalikila mwacangu?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani