LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb23 November tsa. 12
  • Kodi Mbili Yanu ili Ngati ya Yobu?

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Kodi Mbili Yanu ili Ngati ya Yobu?
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2023
  • Nkhani Zofanana
  • “Yembekezela Yehova”
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2022
  • Kodi Yobu Anali Ndani?
    Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2023
mwb23 November tsa. 12
Yobu ali pa cipata ca mzinda ndipo akupatsa cakudya mzimayi wosauka na mwana wake.

Yobu akuonetsa cikondi cosasintha kwa anthu ovutika

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Kodi Mbili Yanu ili Ngati ya Yobu?

Anthu okhala naye pafupi anali kumulemekeza (Yobu 29:​7-11)

Yobu anali kudziŵika na khalidwe loonetsa cikondi cosasintha kwa anthu ovutika (Yobu 29:​12, 13; w02 5/15 22 ¶19; onani cithunzi ca pacikuto)

Yobu anaonetsa kuti anali wacilungamo (Yobu 29:14; it-1 655 ¶10)

Zithunzi: Mlongo wacitsikana akuthandiza ena. 1. Wagwililila mlongo wokalamba pamene akuyenda. 2. Akumvetsela pamene mlongo wina akumuuza mavuto ake. 3. Iye pamodzi na mlongo wina akulalikila mzimayi amene akuyenda na galu wake. 4. Akupatsa cakudya alendo kunyumba kwake.

Mbili yabwino ni yamtengo wapatali. (w09 2/1 15 ¶3-4) Mbili yabwino imapangika munthu akakhala akuonetsa khalidwe labwino kwa nthawi yaitali.

DZIFUNSENI KUTI, ‘Kodi nimadziŵika na makhalidwe otani?’

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani