LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb23 November tsa. 14
  • Zimene Zinathandiza Yobu Kukhalabe Woyela

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Zimene Zinathandiza Yobu Kukhalabe Woyela
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2023
  • Nkhani Zofanana
  • “Yembekezela Yehova”
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2022
  • Pewani Zinthu Zopanda Pake
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2021
  • Kodi Yobu Anali Ndani?
    Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
  • ‘Madalitso Onsewa Adzakupeza’
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2021
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2023
mwb23 November tsa. 14

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Zimene Zinathandiza Yobu Kukhalabe Woyela

Yobu anacita pangano na maso ake (Yobu 31:1; w10 4/15 21 ¶8)

Yobu anaganizila zotulukapo za kucita coipa (Yobu 31:​2, 3; w08 9/1 11 ¶4)

Iye anali kukumbukila kuti Yehova amaona khalidwe lake (Yobu 31:4; w10 11/15 5-6 ¶15-16)

M’bale wayang’ana kumbali ponyansidwa na zimene waona pa kompyuta yake ndipo mwamsanga akuitseka.

Kukhala woyela kumatanthauza kukhala waukhondo ndiponso wosaipitsidwa, osati kunja kokha koma na mkati momwe. Timafuna kukhala woyela na mumtima momwe.—Mat. 5:28.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani