LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • wp25 na. 1 tsa. 2
  • Mawu Oyamba

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Mawu Oyamba
  • Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawila)—2025
  • Nkhani Zofanana
  • Mmene Nkhondo Zimatikhudzila Tonsefe
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawila)—2025
  • Cifukwa Cake Nkhondo Zikupitilizabe Kucitika
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawila)—2025
Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawila)—2025
wp25 na. 1 tsa. 2

Mawu Oyamba

Kodi mumalakalaka kukhala m’dziko lopanda nkhondo komanso ciwawa? N’zimene ambili amafuna. Koma amaona kuti n’zosatheka. Baibo imatiuza cifukwa cake anthu alephela kuthetsa nkhondo. Imapelekanso maumboni otsimikizila kuti n’zotheka kukhala ndi mtendele padziko lonse, ndiponso kuti zimenezi zidzacitikadi posacedwa.

M’magazini ino, mawu akuti “nkhondo” akukamba za kumenyana pakati pa magulu a nkhondo pa zifukwa za ndale. Maina a anthu ena amene achulidwa m’magazini ino asinthidwa.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani