LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • w25 July tsa. 32
  • Muziwelenga Kuti Mugawileko Ena

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Muziwelenga Kuti Mugawileko Ena
  • Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2025
  • Nkhani Zofanana
  • Pezani Cuma Cauzimu Comwe Mungaseŵenzetse
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2024
  • Mfundo Yothandiza Pa Kuŵelenga Kwanu
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2023
  • Kodi Ena Mungawauzeko Bwanji Uthenga Wabwino?
    Kondwelani Na Moyo Kwamuyaya!—Maphunzilo a Baibo Okambilana Komanso Zocita
Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2025
w25 July tsa. 32

MFUNDO YOTHANDIZA PA KUWELENGA KWANU

Muziwelenga Kuti Mugawileko Ena

Kuwelenga kumatitsitsimula. Koma timapindula mokulilapo tikagawilako ena mfundo za coonadi zimene tapeza. Miyambo 11:25 imati: “Amene amatsitsimula ena nayenso adzatsitsimulidwa.”

Tikafotokozelako ena zimene tapeza, zimakhala zosavuta kwa ifeyo kukumbukila zimene tawelenga ndipo timazamitsanso cidziwitso cathu. Timakhala osangalala kugawilako ena mfundo zimene tapeza podziwa kuti zingawalimbikitse.​—Mac. 20:35.

Yesani kucita izi: Mlungu ukubwelawu, yesani kupeza mpata wofotokozelako ena zimene mwaphunzila. Mungacite izi kwa wacibale wanu, kwa m’bale kapena mlongo wa mu mpingo mwanu, kwa mnzanu wa ku nchito kapena wa ku sukulu, kwa aneba anu, kapenanso kwa amene mungakumane nawo mu ulaliki. Yesani kufotokoza zimenezo m’mawu anuanu, m’njila yosavuta kumva, komanso momveka bwino.

Kumbukilani: Muzigawilako ena zimene mwaphunzila n’colinga cowalimbikitsa osati pofuna kudzionetsela.​—1 Akor. 8:1.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani