LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 112
  • Yehova, Mulungu wa Mtendele

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Yehova, Mulungu wa Mtendele
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Yehova Ndi Mulungu Wamtendere
    Imbirani Yehova
  • Mtendele Kodi Mungaupeze Bwanji?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2018
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 112

NYIMBO 112

Yehova, Mulungu wa Mtendele

Yopulinta

(Afilipi 4:9)

  1. 1. M’lungu mwalonjeza,

    Kutipatsa mtendele.

    Tipempha mutithandize,

    Tikulitse mtendele.

    Cikhulupililo

    Cathu mwa Yesu Khristu,

    Catithandiza kukhala

    Pamtendele na imwe.

  2. 2. Titsogoleleni,

    Ndipo mutiteteze

    Na Mau na mzimu wanu,

    Mu dziko lamdimali.

    Tipemphela kuti

    Imwe mutithandize

    Kuti tisunge mtendele

    Pakati pa abale.

  3. 3. Mwatisonkhanitsa,

    Kumwamba na padziko,

    Mwa mzimu tagwilizana,

    Polengeza Ufumu.

    Mu Ufumu wanu,

    Simudzakhala nkhondo,

    Olungama adzakhala

    Pa mtendele kosatha.

(Onaninso Sal. 4:8; Afil. 4:6, 7; 1 Ates. 5:23.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani