LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 150
  • Funani Cipulumutso ca Mulungu

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Funani Cipulumutso ca Mulungu
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Bwerani kwa Mulungu Kuti Mupulumuke
    Imbirani Yehova
  • Ufumu wa Yehova Wayamba Kulamulira
    Imbirani Yehova
  • Ulamulilo wa Yehova Wayamba
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Dalitsani Msonkhano Wathu!
    Imbirani Yehova
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 150

NYIMBO 150

Funani Cipulumutso ca Mulungu

Yopulinta

(Zefaniya 2:3)

  1. 1. Mitundu ya dziko

    Itsutsana na Yesu.

    Nthawi ya kulamulila,

    Kwa anthuwo inatha.

    Tsopano Ufumu

    Wa Yehova wafika.

    Khristu adzaŵafafaniza

    Adani ake onse.

    (KOLASI)

    Funani Yehova M’lungu,

    Na cipulumutso cake.

    Imwe imani

    Ku mbali yake,

    Ndipo khulupilikani.

    Adzakupulumutsani

    Na dzanja lake.

  2. 2. Tsopano ni nthawi,

    Yoti anthu asankhe.

    Kumvela olo kukana

    Za uthenga wabwino.

    Mayeselo athu

    Olo ativutitse

    Yehova ‘dzatisamalila.

    Amamva mapemphelo.

    (KOLASI)

    Funani Yehova M’lungu,

    Na cipulumutso cake.

    Imwe imani

    Ku mbali yake,

    Ndipo khulupilikani.

    Adzakupulumutsani

    Na dzanja lake.

(Onaninso 1 Sam. 2:9; Sal. 2:2, 3, 9; Miy. 2:8; Mat. 6:33.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani