LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 113
  • Mtendele Wathu

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Mtendele Wathu
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Mtendere Wathu Wamtengo Wapatali
    Imbirani Yehova
  • Mtendele Kodi Mungaupeze Bwanji?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2018
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 113

NYIMBO 113

Mtendele Wathu

Yopulinta

(Yohane 14:27)

  1. 1. Yehova, ‘Tate wathu,

    Ni wamtendele.

    Adzathetsadi nkhondo,

    Zonse pa dziko.

    Kalonga wa Mtendele,

    Ni Mwana wake.

    Iye adzabweletsa,

    Mtendele konse.

  2. 2. Mikangano, ukali,

    Zonse tasiya.

    Ise sitinyamula,

    Zida za nkhondo.

    Timakhululukila,

    Otilakwila.

    Monga nkhosa za Yesu,

    Ndise ofatsa.

  3. 3. Anthu onse aone;

    Mtendele wathu.

    Ndipo adzatamanda,

    Mulungu wathu.

    Tisamale za ena,

    M’zocita zathu.

    Tidzaonetsa kuti

    Ndise a M’lungu.

(Onaninso Sal. 46:9; Yes. 2:4; Yak. 3:17, 18.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani