LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 147
  • Lonjezo la Moyo Wamuyaya

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Lonjezo la Moyo Wamuyaya
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Mulungu Watilonjeza Moyo Wosatha
    Imbirani Yehova
  • Khulupilila Coonadi Iwe Mwini
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Khalani ndi Moyo Wopambana
    Imbirani Yehova
  • Inuyo Panokha Muzikonda Kwambiri Choonadi
    Imbirani Yehova
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 147

NYIMBO 147

Lonjezo la Moyo Wamuyaya

Yopulinta

(Salimo 37:29)

  1. 1. Mulungu watilonjeza,

    Moyo wokondweletsa.

    Ngati ticita zabwino,

    Tidzaulandila.

    (KOLASI)

    Moyo wamuyaya,

    M’lungu walonjeza,

    Iye sanganame,

    Zidzacitika.

  2. 2. Ana onse a Yehova,

    Adzakhala angwilo.

    Mu Ufumu wa Mulungu,

    Tidzasangalala.

    (KOLASI)

    Moyo wamuyaya,

    M’lungu walonjeza,

    Iye sanganame,

    Zidzacitika.

  3. 3. Posacedwa’pa Mulungu,

    Adzaukitsa anthu.

    Mitundu yonse ya anthu,

    Idzadalitsika.

    (KOLASI)

    Moyo wamuyaya,

    M’lungu walonjeza,

    Iye sanganame,

    Zidzacitika.

(Onaninso Yes. 25:8; Luka 23:43; Yoh. 11:25; Chiv. 21:4.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani