LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 11
  • Cilengedwe Citamanda Mulungu

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Cilengedwe Citamanda Mulungu
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Zakumwamba Zilengeza Ulemelelo wa Mulungu
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Zakumwamba Zimalengeza Ulemerero wa Mulungu
    Imbirani Yehova
  • Pemphelo Langa Lodzipelekela kwa Mulungu
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Phunzilani Zambili za Yehova Poyang’ana Cilengedwe Cake
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2023
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 11

NYIMBO 11

Cilengedwe Citamanda Mulungu

Yopulinta

(Salimo 19)

  1. 1. Cilengedwe canu M’lungu wathu,

    Ni camphamvu, ni cosangalatsa.

    Cilengeza ucifumu wanu,

    Cimapatsa anthu onse nzelu.

    Cilengeza ucifumu wanu,

    Cimapatsa anthu onse nzelu.

  2. 2. Malamulo anu ni oona,

    Nthawi zonse timawadalila.

    Mau anu amatithandiza—

    Nthawi zonse kukhala anzelu.

    Mau anu amatithandiza—

    Nthawi zonse kukhala anzelu.

  3. 3. Ni dalitso kulambila imwe,

    Kuyeletsa dzina lanu M’lungu.

    Tikamvela malamulo anu,

    Tidzapeza moyo wamuyaya.

    Tikamvela malamulo anu,

    Tidzapeza moyo wamuyaya.

(Onaninso Sal. 12:6; 89:7; 144:3; Aroma 1:20)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani