LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 29
  • Yendani ndi Mtima Wosagawanika

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Yendani ndi Mtima Wosagawanika
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • N’dzayenda mu Umphumphu Wanga
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Khalanibe na Mtima Wamphumphu!
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2019
  • Cimwemwe Cathu Camuyaya
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Tikuyamikani Cifukwa ca Dipo
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 29

Nyimbo 29

Yendani ndi Mtima Wosagawanika

(Salmo 26)

1. Mundiweruzetu Mbuye wanga;

Onani kuti ndimakudalirani.

Ndisanthuleni ndi kundiyesa;

Konzani mtima wanga, mundidalitse.

(KOLASI)

Koma ine, Ndatsimikizadi

Kusonyeza mtima Wosagawanika

2. Sindikhala pa anthu achabe.

Ndidana ndi anthu onyoza cho’nadi.

Musandichotsetu ndi ochimwa

Kapena ndi anthu okonda ziphuphu.

(KOLASI)

Koma ine, Ndatsimikizadi

Kusonyeza mtima Wosagawanika

3. Ndikonda kukhala m’nyumba yanu.

Ndidzachirikiza kulambira kwanu.

Ndidzayendadi kuguwa lanu,

Pokuyamikani mokweza kwambiri.

(KOLASI)

Koma ine, Ndatsimikizadi

Kusonyeza mtima Wosagawanika

(Onaninso Sal. 25:2.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani