LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 68
  • Pemphero la Munthu Wovutika

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Pemphero la Munthu Wovutika
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Pemphelo la Munthu Wovutika
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Mulungu Imvani Pemphero Langa
    Imbirani Yehova
  • Mvelani Pemphelo Langa Conde
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nilimbitseni Mtima
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 68

Nyimbo 68

Pemphero la Munthu Wovutika

(Salimo 4:1)

1. Yehova ndapempha:

“Imvani pemphero langa.”

Zilonda zanga zakula

Sizipola msanga.

Kuvutika ndi maganizo

Kwandifoola.

Ndikomereni mtima

Mulungu wotonthoza.

(KOLASI)

Ndidzutseni. Ndichizeni

Nkhawa zanga zichotseni.

Pa mavuto n’thandizeni,

Yehova ndilimbitseni.

2. Ndikafo’ka

Mawu anu amanditonthoza

Kwambiri,

Moti sindingathe kufotokoza.

Ndidziwe kuti,

Chikondi chanu ndi chosatha

Ndiponso n’chachikulu

Kuposa mtima wanga.

(KOLASI)

Ndidzutseni. Ndichizeni

Nkhawa zanga zichotseni.

Pa mavuto n’thandizeni,

Yehova ndilimbitseni.

(Onaninso Sal. 42:6; 119:28; 2 Akor. 4:16; 1 Yoh. 3:20.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani