LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 3
  • “Mulungu Ndiye Chikondi”

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • “Mulungu Ndiye Chikondi”
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • “Mulungu Ndiye Cikondi”
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Cikondi Khalidwe Lamtengo Wapatali
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2017
  • Musalole Kuti Cikondi Canu Cizilale
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2017
  • “Uzikonda Yehova Mulungu Wako”
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2014
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 3

Nyimbo 3

“Mulungu Ndiye Chikondi”

(1 Yohane 4:7, 8)

1. Mulungu ndiye chikondi,

Wati: ‘Yendani nane.’

Pokonda M’lungu ndi mnansi,

Tizichita zabwino.

Tikatero tidzakondwa;

Tidzapezanso moyo.

Tiyenitu tisonyeze

Chikondi ngati Khristu.

2. Chikondi chimathandiza

Kuchita zabwinodi.

Tikalakwa, amatithandiza

kupeza mphamvu.

Chikondi chilibe nsanje

Koma chimapirira.

Tikamakonda abale,

Tidzadalitsidwadi.

3. Musalole kuti mkwiyo

Ukutsogolereni.

Khulupirirani M’lungu;

Adzakuphunzitsani

Kukonda M’lungu ndi mnansi,

Chikondi chenicheni.

Tizisonyeza anzathu

Chikondi cha Mulungu.

(Onaninso Maliko 12:30, 31; 1 Akor. 12:31–13:8; 1 Yoh. 3:23.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani