LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 127
  • Malo Odziwika ndi Dzina Lanu

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Malo Odziwika ndi Dzina Lanu
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Malo a Dzina Lanu
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • M’patseni Ulemelelo Yehova
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Mvelani Pemphelo Langa Conde
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Mulungu Imvani Pemphero Langa
    Imbirani Yehova
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 127

Nyimbo 127

Malo Odziwika ndi Dzina Lanu

(1 Mbiri 29:16)

1. Yehova kukumangirani

Nyumbayi ndi mwayi wathu.

Tikuipereka tsopano

Lidziwike dzina lanu.

Zimene tingakupatseni

Zinalitu kale zanu.

Luso, ntchito ndi chuma chathu

Timakupatsani inu.

(KOLASI)

Tikupereka malowa

Kuti mudziwikedi.

Tikupereka malowa

Chonde alandireni.

2. Tikulemekeza inuyo

Pokutamandani pano,

Landirani ulemerero

Tikamachuluka muno.

Malowa tikukupatsani

Tidzawasamalirabe.

Ndipo apereke umboni

Inde mpaka kalekale.

(KOLASI)

Tikupereka malowa

Kuti mudziwikedi.

Tikupereka malowa

Chonde alandireni.

(Onaninso 1 Maf. 8:18, 27; 1 Mbiri 29:11-14; Mac. 20:24.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani