LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 94
  • Tiyamikila Mau a Mulungu

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Tiyamikila Mau a Mulungu
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Tikuyamikira Mulungu Kuti Anatipatsa Mawu Ake
    Imbirani Yehova
  • “Muziyamika pa Ciliconse”
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2019
  • Malemba Anauziridwa ndi Mulungu
    Imbirani Yehova
  • Phunzitsani Mau a Mulungu
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 94

NYIMBO 94

Tiyamikila Mau a Mulungu

Yopulinta

(Afilipi 2:16)

  1. 1. Tikuyamikani Atate wathu,

    Cifukwa mwatipatsa Mau anu.

    Amatitsogolela atipatsa nzelu.

    Coonadi cake catimasula.

  2. 2. Mau anu M’lungu, ali na mphamvu.

    Akhudza zolinga za mtima wathu.

    Mfundo zanu, Yehova, zitipatsa nzelu.

    Zititsogolela m’zocita zathu.

  3. 3. Mau anu M’lungu, atithandiza.

    Kuphunzila kwa aneneli anu.

    Conde tithandizeni tikhale olimba.

    Tikuyamikani Mulungu wathu.

(Onaninso Sal. 19:9; 119:16, 162; 2 Tim. 3:16; Yak. 5:17; 2 Pet. 1:21.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani