LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 68
  • Fesani Mbewu za Ufumu

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Fesani Mbewu za Ufumu
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Fesani Mbewu za Ufumu
    Imbirani Yehova
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 68

NYIMBO 68

Fesani Mbewu za Ufumu

Yopulinta

(Mateyu 13:4-8)

  1. 1. Bwelani kwa Ambuye Yesu,

    Kuti museŵenze naye.

    Iye adzakuthandizani,

    Adzakutsogolelani.

    Mbewu za co’nadi zimakula

    M’mitima ya omvetsela.

    Modzipeleka citani mwakhama

    Nchito imene mwapatsidwa.

  2. 2. Kuti nchito iyende bwino

    Pafunika khama lanu.

    Muthandizenso omvetsela

    Kuti akonde co’nadi.

    Athandizeni kudziŵa kuti

    Angapilile mavuto.

    Ngati mwaona mbewu za co’nadi

    Zikula mudzasangalala.

(Onaninso Mat. 13:19-23; 22:37.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani