LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 118
  • Landiranani

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Landiranani
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Tilandilane Wina Ndi Mnzake
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Alandileni!
    Utimiki Wathu wa Ufumu—2013
  • Alandileni Bwino
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
  • Landilani Alendo
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 118

Nyimbo 118

Landiranani

(Aroma 15:7)

1. Takulandirani inu nonse.

Mwasonkhana kuti m’phunzire.

Cho’nadi M’lungu amatipatsa

Timavomera akamatiitana.

2. Tikuyamikira abalewa

Chifukwa amatilandira.

Ndi amenewa tizikondana,

Tilandirenso ena odzasonkhana.

3. Aliyense akuitanidwa

Ndi M’lungu kudzaphunzitsidwa.

M’lungu watikokera kwa Iye

Choncho landiranani ndi mtima wonse.

(Onaninso Yoh. 6:44; Afil. 2:29; Chiv. 22:17.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani