LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 133
  • Bwerani kwa Mulungu Kuti Mupulumuke

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Bwerani kwa Mulungu Kuti Mupulumuke
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Funani Cipulumutso ca Mulungu
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Ufumu wa Yehova Wayamba Kulamulira
    Imbirani Yehova
  • Ulamulilo wa Yehova Wayamba
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Dalitsani Msonkhano Wathu!
    Imbirani Yehova
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 133

Nyimbo 133

Bwerani kwa Mulungu Kuti Mupulumuke

(Zefaniya 2:3)

1. Mitundu ya anthu

Ikutsutsadi Yesu.

Nthawi yawo yolamula

Yatha watero M’lungu.

Ufumu wayamba

Ndipo wakhazikika.

Adani onse apadziko

Khristu adzawaphwanya.

(KOLASI)

Bweranitu kwa Yehova

Kuti mudzapulumuke.

Mumudalire,

M’khulupirike,

Khalani kumbali yake.

Adzakupulumutsani

Ndi mphamvu zake.

2. Sankhani tsopano

Anthunu apadziko

Kumvera kaya kukana

Uthengawu wabwino.

Ngakhale mavuto

Tingakumane nawo

Yehova amasamalira

Tikapempha thandizo.

(KOLASI)

Bweranitu kwa Yehova

Kuti mudzapulumuke.

Mumudalire,

M’khulupirike,

Khalani kumbali yake.

Adzakupulumutsani

Ndi mphamvu zake.

(Onaninso 1 Sam. 2:9; Sal. 2:2, 3, 9; Miy. 2:8; Mat. 6:33.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani