LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb16 October tsa. 7
  • “Phunzitsa Mwana m’Njila Yomuyenelela”

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • “Phunzitsa Mwana m’Njila Yomuyenelela”
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
  • Nkhani Zofanana
  • Mmene Mungalangile Ana Anu
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2014
  • Cilango Ni Umboni Wakuti Mulungu Amatikonda
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2018
  • Cilango Cimaonetsa Cikondi ca Yehova
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2021
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
mwb16 October tsa. 7

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU | MIYAMBO 22-26

“Phunzitsa Mwana m’Njila Yomuyenelela”

Mayi aŵelengela mwana wake wamkazi mpukutu pamene tate na mwana wamwamuna aumba mbiya

M’buku la Miyambo muli malangizo othandiza kwa makolo. Kuwongola mtengo ukali waung’ono kumathandiza kuti ukule woongoka. Mogwilizana na zimenezi, makolo afunika kuphunzitsa ana awo akali aang’ono. Akacita conco, adzathandiza anawo kuti akadzakula akakhale na mtima wofuna kutumikila Yehova.

22:6

  • Munthu amangilila kamtengo ku mtengo waung’ono womela

    Kuphunzitsa bwino ana kumafuna nthawi na khama

  • Makolo afunika kupeleka citsanzo cabwino kwa ana awo. Afunikanso kuwalangiza, kuwacenjeza, kuwalimbikitsa, ndi kuwapatsa cilango

22:15

  • Cilango ndi kuphunzitsa kwacikondi kumene kumathandiza mwana kusintha maganizo na mtima

  • Cilango cimene ana amafunikila cimakhala cosiyana-siyana

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani