LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb16 December tsa. 7
  • Dziko Lapansi Lidzadzala na Ŵanthu Odziŵa Yehova

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Dziko Lapansi Lidzadzala na Ŵanthu Odziŵa Yehova
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
  • Nkhani Zofanana
  • “Tidzaonana M’Paradaiso!”
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2018
  • Kodi Mwasandulika?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2013
  • Ufumu Ukwanilitsa Cifunilo ca Mulungu Padziko Lapansi
    Ufumu wa Mulungu Ukulamulila
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
mwb16 December tsa. 7

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU | YESAYA 11-16

Dziko Lapansi Lidzadzala na Ŵanthu Odziŵa Yehova

Kamwana kali m’paradaiso kaseŵela na nyama za kusanga

11:6-9

Kukwanilitsika kwa ulosiwu kwa Aisiraeli

  • Aisiraeli paulendo wawo wocoka ku ukapolo ku Babulo, ndiponso pamene anafika ku dziko lakwawo, sanafunikile kucita mantha ndi nyama za m’sanga, kapena anthu olusa monga nyama za m’sanga.—Ezara 8:21, 22.

Kukwanilitsika kwake masiku ano

  • Anthu asintha umunthu wawo cifukwa codziŵa Yehova. Anthu amene kale anali aciwawa akhala amtendele. Kudziŵa Mulungu kwacititsa kuti tikhale m’paradaiso wauzimu padziko lonse lapansi.

Kukwanilitsika kwa ulosiwu mtsogolo

  • Monga mmene Mulungu anali kufunila paciyambi, dziko lonse lidzasinthiwa na kukhala malo otetezeka, paradaiso wa mtendele. Palibe colengedwa cimene cidzayofya cinzake, munthu kapena nyama.

Paulo anasintha cifukwa codziŵa Mulungu

  • Pamene anali mfalisi, anali na makhalidwe monga a cilombo. —1 Tim. 1:13.

  • Kudziŵa zinthu molongosoka kunasintha umunthu wake. —Akol. 3:8-10.

Mtumwi Paulo anasintha umunthu waukali na kukhala wofatsa
    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani