LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb18 December tsa. 3
  • Paulo na Baranaba Apanga Ophunzila Kumadela Akutali

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Paulo na Baranaba Apanga Ophunzila Kumadela Akutali
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
  • Nkhani Zofanana
  • Cikhristu Cifalikila Kumadela Akutali
    Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
mwb18 December tsa. 3
Paulo na Baranaba aimilila pamaso pa Serigio Paulo

Paulo na Baranaba aimilila pamaso pa Serigio Paulo

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | MACHITIDWE 12-14

Paulo na Baranaba Apanga Ophunzila Kumadela Akutali

13:12, 48; 14:1, 21, 22

Ngakhale kuti Paulo na Baranaba anatsutsidwa mwamphamvu, anacita khama kuthandiza anthu ofatsa kukhala Akhristu

  • Iwo analalikila anthu a zikhalidwe zosiyana-siyana

  • Analimbikitsa ophunzila atsopano kuti “akhalebe m’cikhulupililo”

Sitingaadziŵe anthu a “maganizo abwino” amene angayenelele moyo wosatha ngati sitinawalalikile, mwinanso mobweleza-bweleza. Conco, timalalikila aliyense mopanda tsankho.

Kodi wiki ino ningapemphe ndani kuti nizim’phunzitsa Baibo?

Kodi Akhristu anzanga ningawalimbikitse bwanji kuti “akhalebe m’cikhulupililo”?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani