LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 77
  • Kuwala m’Dziko la Mdima

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Kuwala m’Dziko la Mdima
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Kuwala m’Dziko la Mdima
    Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 77

NYIMBO 77

Kuwala m’Dziko la Mdima

Yopulinta

(2 Akorinto 4:6)

  1. 1. Kuwala kukuunika,

    m’Dziko la mdimali.

    Tiuza anthu uthenga,

    Wa ciyembekezo.

    (KOLASI)

    Uthenga wa M’lungu

    Umawala kwambili,

    m’Dziko la mdimali—

    Umapatsa anthu,

    Onse ciyembekezo—

    Mwa Mulungu.

  2. 2. Ogona agalamuke,

    Si nthawi yogona.

    Auke, tiŵalimbitse.

    Tiŵapemphelele.

    (KOLASI)

    Uthenga wa M’lungu

    Umawala kwambili,

    m’Dziko la mdimali—

    Umapatsa anthu,

    Onse ciyembekezo—

    Mwa Mulungu.

(Onaninso Yoh. 3:19; 8:12; Aroma 13:11, 12; 1 Pet. 2:9.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani