LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • snnw nyimbo 143 tsa. 8
  • Kuwala m’Dziko la Mdima

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Kuwala m’Dziko la Mdima
  • Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Nkhani Zofanana
  • Kuwala m’Dziko la Mdima
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Munapeleka Mwana Wanu Wobadwa Yekha
    Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Tikuyamikani Cifukwa ca Dipo
    Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Ana a Mulungu Adzaonekela
    Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
Onaninso Zina
Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
snnw nyimbo 143 tsa. 8

Nyimbo 143

Kuwala m’Dziko la Mdima

Yopulinta

(2 Akorinto 4:6)

  1. Kuwala kukuunika,

    m’Dziko la mdimali.

    Tiuza anthu uthenga

    wa ciyembekezo.

    (KOLASI)

    Uthenga wa M’lungu

    Umawala kwambili,

    m’Dziko la mdimali—

    Umapatsa anthu,

    Onse ciyembekezo—

    Mwa Mulungu.

  2. Ogona agalamuke

    Si nthawi yogona.

    Auke, tiwalimbitse.

    Tiŵapemphelele.

    (KOLASI)

    Uthenga wa M’lungu

    Umawala kwambili,

    m’Dziko la mdimali—

    Umapatsa anthu,

    Onse ciyembekezo—

    Mwa Mulungu.

(Onaninso Yoh. 3:19; 8:12; Aroma 13:11, 12; 1 Pet. 2:9.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani