LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb20 June tsa. 8
  • Mungakwanitse Kulalikila na Kuphunzitsa!

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Mungakwanitse Kulalikila na Kuphunzitsa!
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
  • Nkhani Zofanana
  • Zimene Zingakuthandizeni Ngati Utumiki Wanu Watha
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2019
  • ‘Limba Mtima, Ugwile Nchito Mwamphamvu’
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2017
  • Kodi Uthenga Wabwino Umalalikidwa Motani?
    Kondwelani Na Moyo Kwamuyaya!—Maphunzilo a Baibo Okambilana Komanso Zocita
  • Kukhala Wolimba Mtima Sikovuta
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2021
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
mwb20 June tsa. 8

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

Mungakwanitse Kulalikila na Kuphunzitsa!

Mose poyamba anakayikila zakuti angakwanitse kucita nchito imene Yehova anamupatsa. (Eks. 4:10, 13) Kodi na imwe munadzikayikilapo? Kodi mukuphunzila Baibo na Mboni za Yehova? Kodi mumadzifunsa ngati mudzakwanitsa kulalikila ku nyumba na nyumba? Kapena ndimwe wacicepele amene amacita mantha kulalikila ku sukulu. Kapena mwina mumacita mantha kutengako mbali pa ulaliki wa pa foni kapena wapoyela. Pemphani Yehova kuti akupatseni mphamvu yake ya mzimu woyela. (1 Pet. 4:11) Khalani na cidalilo cakuti angakuthandizeni pa nchito iliyonse imene wakupatsani.—Eks. 4:11, 12.

TAMBANI VIDIYO YAKUTI KHALANI OLIMBA MTIMA . . . INU OFALITSA, NDIYENO YANKHANI MAFUNSO OTSATILAWA:

  • Kodi ni vuto lanji limene mlongo Aoyama anakumana nalo?

  • Kodi n’ciani cinam’thandiza kupeza mphamvu komanso kukhala wolimba mtima?—Yer. 20:7-9

  • Kodi anapindula bwanji powonjezela zocita potumikila Yehova?

  • Kodi Yehova angakuthandizeni kuthana na mavuto ati mu ulaliki?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani