LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 40
  • Kodi Ndife a Ndani?

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Kodi Ndife a Ndani?
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Kodi Ndife Anthu a Ndani?
    Imbirani Yehova
  • Kodi Ndinu ‘Wokonzeka Kumvela’?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2023
  • Adzakulimbitsa
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Khalani Omvera Kuti Mulandire Madalitso
    Imbirani Yehova
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 40

NYIMBO 40

Kodi Ndife a Ndani?

Yopulinta

(Aroma 14:8)

  1. 1. M’lungu wako n’ndani?

    Umamvelela uti?

    Ni uja amene umam’gwadila,

    Na kum’tumikila.

    Milungu iŵili,

    Sungaitumikile.

    Sankhapo cabe Mulungu mmodzi

    Amene umakonda.

  2. 2. M’lungu wako n’ndani?

    Udzamvelela uti?

    Cili kwa iwe, sankha wekha,

    Wabodza olo woona.

    Wasankha kumvela

    Mafumu a dzikoli

    Olo wasankha kumvela M’lungu,

    Na kucita zabwino?

  3. 3. M’lungu wanga n’ndani?

    Nidzamvela Yehova.

    Nidzam’tumikila mokondwa

    Komanso modzipeleka.

    Mokhulupilika

    Nidzayenda na M’lungu.

    Nidzam’tumikila nthawi zonse,

    Na kumulemekeza.

(Onaninso Yos. 24:15; Sal. 116:14, 18; 2 Tim. 2:19.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani