LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 44
  • Pemphelo la Munthu Wovutika

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Pemphelo la Munthu Wovutika
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Pemphero la Munthu Wovutika
    Imbirani Yehova
  • Mulungu Imvani Pemphero Langa
    Imbirani Yehova
  • Mvelani Pemphelo Langa Conde
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nilimbitseni Mtima
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 44

NYIMBO 44

Pemphelo la Munthu Wovutika

Yopulinta

(Salimo 4:1)

  1. 1. Yehova, nipempha mvelani pemphelo langa.

    Nkhawa zanga zanivutitsa; nithandizeni.

    Navutika mu maganizo ndipo nafo’ka.

    O Yehova nipempha; conde munisamale.

    (KOLASI)

    N’thandizeni kupilila.

    Nkhawa zanga zicotseni.

    Nikafo’ka na mavuto

    Yehova nilimbitseni.

  2. 2. Mau anu amanitonthoza nikafo’ka,

    Niyamikila moti siningafotokoze.

    N’thandizeni kudziŵa kuti mumanikonda.

    Nikhulupilila kuti mudzanithandiza.

    (KOLASI)

    N’thandizeni kupilila.

    Nkhawa zanga zicotseni.

    Nikafo’ka na mavuto

    Yehova nilimbitseni.

(Onaninso Sal. 42:6; 119:28; Aroma 8:26; 2 Akor. 4:16; 1 Yoh. 3:20.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani