LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 62
  • Kodi Ndife Anthu a Ndani?

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Kodi Ndife Anthu a Ndani?
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Kodi Ndife a Ndani?
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Khalani ndi Moyo Wopambana
    Imbirani Yehova
  • Lomba Ndise Thupi Limodzi
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Tsopano Ndife Thupi Limodzi
    Imbirani Yehova
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 62

Nyimbo 62

Kodi Ndife Anthu a Ndani?

(Aroma 14:8)

1. Iwe ndi wandani?

Umvera m’lungu uti?

Amene umam’gwadirayo,

Iye ndiye m’lungu wako.

Milungu iwiri

Sungaitumikire,

Sungalambire awiri onse,

Sungakhulupirike.

2. Iwe ndi wandani?

Umvera m’lungu uti?

Zilitu ndi iwe kusankha

Woona mwina wonama.

Kodi Kaisara

Udakamukondabe?

Kapena udzamvera Yehova

N’kuchita ntchito yake?

3. Ine ndi wandani?

Ndidzamvera Yehova.

Atate wanga wakumwamba

Ine ndidzam’sangalatsa.

Anandiwombola

Popatsa mwana wake,

Ndim’lambirabe, Ndi dzina lake

Ndililemekezabe.

(Onaninso Yos. 24:15; Sal. 116:14, 18; 2 Tim. 2:19.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani