Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Numeri 20:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Deuteronomo 8:14, 15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 musakalole kuti mtima wanu ukayambe kunyada+ nʼkukuchititsani kuiwala Yehova Mulungu wanu amene anakutulutsani mʼdziko la Iguputo, mʼnyumba yaukapolo,+ 15 amene anakuyendetsani mʼchipululu chachikulu ndi chochititsa mantha,+ chokhala ndi njoka zapoizoni, zinkhanira ndiponso nthaka youma yopanda madzi. Iye anachititsa kuti madzi atuluke pamwala wolimba,+

  • Nehemiya 9:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Pamene anali ndi njala munawapatsa chakudya chochokera kumwamba+ ndipo pamene anali ndi ludzu munatulutsa madzi pathanthwe.+ Munawauza kuti alowe nʼkutenga dziko limene munalumbira* kuti mudzawapatsa.

  • Salimo 78:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Iye anangʼamba miyala mʼchipululu,

      Anawalola kumwa madziwo mpaka ludzu kutha ngati kuti akumwa madzi amʼnyanja.+

  • Salimo 105:41
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • 1 Akorinto 10:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • 1 Akorinto 10:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani