-
Deuteronomo 8:14, 15Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
14 musakalole kuti mtima wanu ukayambe kunyada+ nʼkukuchititsani kuiwala Yehova Mulungu wanu amene anakutulutsani mʼdziko la Iguputo, mʼnyumba yaukapolo,+ 15 amene anakuyendetsani mʼchipululu chachikulu ndi chochititsa mantha,+ chokhala ndi njoka zapoizoni, zinkhanira ndiponso nthaka youma yopanda madzi. Iye anachititsa kuti madzi atuluke pamwala wolimba,+
-
-
Salimo 78:15Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
15 Iye anangʼamba miyala mʼchipululu,
Anawalola kumwa madziwo mpaka ludzu kutha ngati kuti akumwa madzi amʼnyanja.+
-