Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Levitiko 3:16, 17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Levitiko 4:8-10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Kenako azichotsa mafuta onse a ngʼombe ya nsembe yamachimo, kuphatikizapo mafuta okuta matumbo ndi mafuta onse apamatumbo. 9 Azichotsanso impso ziwiri zomwe zili pafupi ndi chiuno ndi mafuta okuta impsozo. Komanso azichotsa mafuta apachiwindi pamodzi ndi impsozo.+ 10 Zinthu zimenezi zizikhala zofanana ndi zomwe azichotsa pa ngʼombe ya nsembe yamgwirizano.+ Ndipo wansembe aziziwotcha paguwa lansembe zopsereza.

  • 1 Samueli 2:16, 17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Munthuyo akanena kuti: “Yembekeza kaye apsereze mafutawo+ kenako utenge chilichonse chimene ukufuna,” iye ankayankha kuti: “Ayi, ndipatse pompano, apo ayi ndichita kulanda!” 17 Atumikiwa ankachimwira Yehova kwambiri,+ chifukwa sankalemekeza nsembe ya Yehova.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani