Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Ekisodo 29:27, 28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Levitiko 10:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Mudyenso chidale cha nsembe yoyendetsa uku ndi uku ndi mwendo wa gawo lopatulika.+ Muzidyere pamalo amene ayeretsedwa, inuyo, ana anu aamuna ndi ana anu aakazi.+ Muzichita zimenezi chifukwa zinthu zimenezi zaperekedwa kwa inu monga gawo lanu ndi gawo la ana anu kuchokera pa nsembe zamgwirizano za Aisiraeli.

  • Numeri 6:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Wansembeyo aziyendetsa zinthuzo uku ndi uku monga nsembe yoperekedwa kwa Yehova.+ Zinthuzi ziziperekedwa kwa wansembeyo ngati mphatso yopatulika, limodzi ndi chidale cha nsembe yoyendetsa uku ndi uku, komanso mwendo womwe ndi gawo lopatulika.+ Pambuyo pake munthu yemwe anali Mnaziriyo angathe kumwa vinyo.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani