-
Deuteronomo 18:3Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
3 Tsopano zinthu zimene ansembe azidzalandira kuchokera kwa anthu ndi izi: Amene akupereka nsembe ya ngʼombe kapena nkhosa, azipereka kwa wansembe mwendo wakutsogolo, nsagwada ndi chifu.
-