-
Deuteronomo 17:1Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
17 “Musamapereke kwa Yehova Mulungu wanu nsembe ya ngʼombe kapena nkhosa imene ili ndi chilema kapena vuto lililonse, chifukwa idzakhala yonyansa kwa Yehova Mulungu wanu.+
-