-
Oweruza 2:2, 3Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
2 Inuyo musachite pangano ndi anthu okhala mʼdzikoli,+ ndipo mugwetse maguwa awo ansembe.’+ Koma inu simunamvere mawu anga.+ Nʼchifukwa chiyani mwachita zimenezi? 3 Nʼchifukwa chake ndinanena kuti, ‘Sindidzawathamangitsa pamaso panu,+ koma adzakhala msampha wanu,+ ndipo milungu yawo idzakhala ngati nyambo.’”+
-