Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Genesis 10:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Genesis 15:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Genesis 17:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Deuteronomo 4:38
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 38 Anachotsa pamaso panu mitundu yaikulu ndi yamphamvu kuposa inu, kuti akulowetseni mʼdziko lawo nʼkukupatsani kuti likhale cholowa chanu ngati mmene zilili lero.+

  • Yoswa 1:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Dziko lanu lidzayambira kuchipululu kufika ku Lebanoni mpaka kumtsinje waukulu wa Firate, dziko lonse la Ahiti+ mpaka kukafika ku Nyanja Yaikulu* kumadzulo.+

  • Yoswa 14:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Aisiraeli anatenga cholowa chawo mʼdziko la Kanani. Wansembe Eliezara, Yoswa mwana wa Nuni ndi atsogoleri a mafuko a makolo a Aisiraeli ndi amene anawagawira cholowachi.+

  • Yeremiya 3:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Ine ndinkaganiza kuti, ‘Mosangalala ndinakuika pakati pa ana aamuna nʼkukupatsa dziko labwino kwambiri, cholowa chokongola kwambiri pakati pa mitundu ya anthu!’*+ Ndinkaganizanso kuti uzindiitana kuti, ‘Bambo anga!’ ndiponso kuti sudzasiya kunditsatira.

  • Machitidwe 17:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani