Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Deuteronomo 4:42
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 42 Ngati munthu wapha mnzake mwangozi ndipo sanayambe wadanapo naye,+ munthu ameneyu azithawira ku umodzi mwa mizinda imeneyi kuti akhale ndi moyo.+

  • Yoswa 20:2, 3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Yoswa 20:7, 8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Yoswa 21:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Ana a wansembe Aroni anawapatsa mzinda wothawirako munthu amene wapha mnzake,+ wa Heburoni+ ndi malo ake odyetserako ziweto. Anawapatsanso Libina+ ndi malo ake odyetserako ziweto,

  • Yoswa 21:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Anawapatsa mzinda wothawirako munthu amene wapha mnzake,+ wa Sekemu,+ ndi malo ake odyetserako ziweto mʼdera lamapiri la Efuraimu. Anawapatsanso Gezeri+ ndi malo ake odyetserako ziweto,

  • Yoswa 21:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Ana a Gerisoni+ a mʼmabanja a Alevi, anapatsidwa mizinda kuchokera ku hafu ya fuko la Manase. Anawapatsa mzinda wothawirako munthu amene wapha mnzake, wa Golani+ ku Basana ndi malo ake odyetserako ziweto ndiponso Beesitera ndi malo ake odyetserako ziweto. Inalipo mizinda iwiri.

  • Yoswa 21:32
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 32 Kuchokera mʼfuko la Nafitali, anawapatsa mzinda wothawirako+ munthu amene wapha mnzake, wa Kedesi+ ku Galileya ndi malo ake odyetserako ziweto. Anawapatsanso Hamoti-dori ndi malo ake odyetserako ziweto ndiponso Karitani ndi malo ake odyetserako ziweto. Yonse inalipo mizinda itatu.

  • Yoswa 21:36
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 36 Kuchokera mʼfuko la Rubeni, anawapatsa Bezeri+ ndi malo ake odyetserako ziweto, Yahazi ndi malo ake odyetserako ziweto,+

  • Yoswa 21:38
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 38 Kuchokera mʼfuko la Gadi,+ anawapatsa mzinda wothawirako munthu amene wapha mnzake, wa Ramoti ku Giliyadi+ ndi malo ake odyetserako ziweto. Anawapatsanso Mahanaimu+ ndi malo ake odyetserako ziweto,

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani