-
Numeri 3:39Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
39 Amuna onse afuko la Levi amene Mose ndi Aroni anawawerenga, pomvera lamulo la Yehova analipo 22,000. Anawerenga amuna onse kuyambira a mwezi umodzi kupita mʼtsogolo potengera mabanja awo.
-
-
Numeri 3:43Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
43 Ana onse aamuna oyamba kubadwa amene anawawerenga, kuyambira a mwezi umodzi kupita mʼtsogolo, anakwana 22,273.
-