Ekisodo 19:21 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 1 Samueli 6:19 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 19 Koma Mulungu anapha anthu a ku Beti-semesi chifukwa anayangʼana Likasa la Yehova. Anapha anthu 50,070* ndipo anthu anayamba kulira chifukwa Yehova anapha anthu ambiri.+
19 Koma Mulungu anapha anthu a ku Beti-semesi chifukwa anayangʼana Likasa la Yehova. Anapha anthu 50,070* ndipo anthu anayamba kulira chifukwa Yehova anapha anthu ambiri.+