Ekisodo 6:23 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika Numeri 4:33 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 33 Izi ndi zimene mabanja a ana a Merari+ azichita monga mbali ya utumiki wawo pachihema chokumanako. Itamara mwana wa wansembe Aroni,+ ndi amene aziyangʼanira utumiki wawo.” Numeri 7:8 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
33 Izi ndi zimene mabanja a ana a Merari+ azichita monga mbali ya utumiki wawo pachihema chokumanako. Itamara mwana wa wansembe Aroni,+ ndi amene aziyangʼanira utumiki wawo.”