-
Levitiko 7:7Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
7 Lamulo la nsembe yakupalamula ndi lofanana ndi la nsembe yamachimo. Nyama ya nsembeyi izikhala ya wansembe amene wapereka nsembeyo pophimba machimo.+
-