Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Levitiko 4:22, 23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Ngati mtsogoleri+ wachimwa mosadziwa pochita chimodzi mwa zinthu zonse zimene Yehova Mulungu wake analamula kuti asachite ndipo wapalamula, 23 kapena ngati wadziwa kuti wachimwa pochita zinthu zosemphana ndi lamulo, azibweretsa mbuzi yaingʼono yamphongo yopanda chilema, kuti ikhale nsembe yake.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani